Home Featured Dodma ili tcheru ngati madzi angasefukire

Dodma ili tcheru ngati madzi angasefukire

by Peter Dziyende
0 comments

Nthambi yoona za ngozi zogwa mwadzidzi ya Department of Disaster Management Affairs- Dodma yati ili tcheru powonetsetsa kuti katundu ndi miyoyo ya anthu isaonongeke ngati mvula yomwe ikugwa m’madera ena Ingachititse kusefukira kwa madzi.

Masiku apitawa nthambi yowona za nyengo m’dziko muno inalengeza kuti mvula yochuluka igwa m’madera ena a dziko lino kuphatikizapo ku Nkhotakota, ndi Salima mwa ena, sabata ino.

M’mau ake, M’neneri wa bungwe la Dodma, a Chipiliro Khamula ati Dodma yayamba kale kutumiza akatswiri opulumutsa anzawo pa ngozi zogwa mwadzidzi m’maboma omwe ali pa chiopsezo.

You may also like

Leave a Comment

Dzimwe Community Radio is nonprofit making institution currently located behind the Community Resource Centre Hall to the South East of Monkey Bay Airstrip. The radio was established in 1998 initially funded by UNITED NATION EDUCATION SCIENTIFIC AND CULTURE ORGANISATION (UNESCO) to act as a platform where people can discuss issues and find lasting solutions that concern them to achieve sustainable development.

Newsletter

Subscribe my Newsletter for new blog posts, tips & new photos. Let's stay updated!

@2025 – All Right Reserved. MACRA Community Radios

Are you sure want to unlock this post?
Unlock left : 0
Are you sure want to cancel subscription?
-
00:00
00:00
Update Required Flash plugin
-
00:00
00:00