Home Featured Andale Achimayi awapempha kuti alemekezeke Ovota

Andale Achimayi awapempha kuti alemekezeke Ovota

by Peter Dziyende
1 comment

M’khala kale pa ndale a Patricia Kaliati achenjeza amayi omwe akupikisana nawo pa chisankho cha sabata la mawa kuti achepetse kudziyenereza kuti apambana kale chisankhochi ponena kuti kudziyenereza kumachotsa chidwi cha ovota pa chisankho.

Iwo anena izi pamene anali mulendo olemekezeka pa mkumano wa amayi omwe akuyima m’maudindo osiyanasiyana pa chisankhochi ku Wapansi Hotel m’boma la Mangochi.

Malingana ndi a Kaliati “Mukadziyenereza anthu asanakusankheni mulephera chifukwa choti nthawi ya chisankho mabwana ndi anthu ovota, apatseni ulemu ndipo adzakukondani ndikukuvoterani,” atero a Kaliati.

Iwo ati ma udindo a ndale ndi mayitanidwe ndipo alangiza amayiwa kusamala mayankhulidwe, zochitika komanso mavalidwe ponena kuti ngati m’dindo, mayi amakhala chitsanzo kwa atsikana ndi amayi achichepere.

You may also like

1 comment

Richard2853 February 12, 2026 - 1:27 am Reply

Leave a Comment

Dzimwe Community Radio is nonprofit making institution currently located behind the Community Resource Centre Hall to the South East of Monkey Bay Airstrip. The radio was established in 1998 initially funded by UNITED NATION EDUCATION SCIENTIFIC AND CULTURE ORGANISATION (UNESCO) to act as a platform where people can discuss issues and find lasting solutions that concern them to achieve sustainable development.

Newsletter

Subscribe my Newsletter for new blog posts, tips & new photos. Let's stay updated!

@2025 – All Right Reserved. MACRA Community Radios

Are you sure want to unlock this post?
Unlock left : 0
Are you sure want to cancel subscription?
-
00:00
00:00
Update Required Flash plugin
-
00:00
00:00